Skip to main content

AKAPUSA MUDYERE

Misonzi yachimwemwe idatsikira mmasaya mwa Sitelia kuchoka mmaso mwake. Sadathe kukhulupirira kuti loto lake lakwaniritsidwa. Zinali ngati kuti ali mtulo ndipo ali kulota. Chapatali potero Waisoni adakhala chete mkumaonerera mwambo wonse wa ukwati wa mkazi wake wa kale. Adakumbukira mmene amkamutukwanira komanso kumunyoza mkazi yo pa nthawi imene adali limodzi, mtima wake udagunda koposa ndipo anamva kuwawidwa. Kwa iye mkazi anali kalopo koposa ndipo amkakhulupirira kuti kumtchenetsa mkazi Kapena kumuyambitsa bizinesi kunali kutaya nthawi komanso kuononga ndalama chabe. Tsiku liri lonse Sitelia adali akukhala odandaula ndinso kugona ndi njala limodzi ndi ana ake awiri pamene Waisoni adali kupita kuzisangalalo kumene amakadyako mang'ina, zibwente, tchipisi ndi fuloze. Amkapita kunyumba atakhuta ndipo amkangofikira phiii kugona. Khalidwe li mkazi atafika potopa nalo anayamba kuyenda yenda mnamakasaka chakudya cha iye ndi ana ake ndipo waisoni analibe nazo ntchito. Pamene mkazi yu adakali pakati posaka chakudya adakumana ndi chikhwaya chogwira ntchito mu banki, adakondana ndipo ubwenzi udayamba. Kwa miyezi ingapo ubwenzi wawo udakulira ndinso kutentherera koma zonsezi Waisoni sadali kuziwa pakuti samkakhala pakhomo tsiku lonse. Usiku wina mwachidzolowedzi adangodabwa kufika pakhomo mkupedza kuti mkazi wake komanso ana palibe. Adayang'ana muzipinda zonse za mnyumba mo ndipo sadawapedze, adakhala pabalaza mnawadikirira koma mawola awiri adadutsa ndipo iwo sadatulukire, adaganiza zopita kuchipinda kumene iye ndi mkazi wake Sitelia amkagona ndipo adali ozizidwa nkhongono kupedza chibaluwa chomwe mkazi yo adalemba kumusanzika kuti wapita kukaona patsidya la nyanja pamodzi ndi khadi lomuitana ku ukwati omwe mkazi wakeyo adali kuchita lachiweru lomwe lidali kudza. Izi zinamuvuta Waisoni kukhulupirira ndipo lisipa ndi mutu wa ching'alang'ala zidamupedza.  Adakanika kumvetsa kuti mkazi wakeyo wapitadi ndipo adawona kuchedwa kuti lachiweru lifike akazionere yekha ngati zinalidi zoona. Tulo tidamusowa. Adakhala akulingalira komanso Kulira kuti zibwana zake zamuthawitsira mkazi ndi ana omwe. Tsiku lo litafika Wasioni adakonzeka molawira koposa ngati mwina ukwati wo udali wake ndipo adalunjika Ku kachisi imene ukwati wo umkadalitsidwira. Mmimba mudaotcha ndipo adaona ngati chifunga komanso anamva kutentha mthupi mwake monse pamene adawona mkazi wake Sitelia ali mu Velo loyera bwino ngati ngelo, maphodedwe amene adali pa thupi la mkazi yu adamupangitsa Waisoni kubwera mkhwidzi yomwe adakanika kuitula pakuti kupusa kwake mkomwe kudapangitsa kuti ena amulande mkazi.  Adalaka laka atatsatira mkazi wake yo kutsogolo pamene m'busa adafunsa ngati analipo wina oletsa kuti awiri wo asakhale limodzi ngati banja. Koma kunali komuvuta zedi Waisoni kutero pakuti miyendo yake komanso minyewa yonse idali itafooka koposa ndipo mphamvu zoimirira adalibe pakuti adali kuopa kuti atha kuchitira chimbuzi mukachisi mo kaamba ka mantha komanso mkwiyo ndi manyazi omwe adali nawo. Apa mpamene Waisoni adadzindikira kuti munthu di akapusa amadyeredwa ndithu ingakhale mkazi amene.. CHENJERA!!!!


THE END!

Comments

  1. Wow!!! You have put a lot of work into this piece and phunziro lalikulu heavy. Keep up the good work 💪💪💪

    ReplyDelete

Post a Comment

Popular posts from this blog

I LIVE

  The phase I was in weeks ago made me question my existence on earth “perhaps, has my time elapsed?” I have escaped a number of accidents for two weeks in a roll. I was on bed rest. Got back on feet and faced yet another accident day after day “I thought my life has come to an end.” “I could barely let food pass my throat; the fear-anxiety and the stress all over it of what becomes of me the next day was too much for my mind” “is death beckoning me?” I asked myself a couple of random questions just to be sure I was on a right spot - safe and sane “I must repent.” “Change my ways, stay sane even in the midst of the rumbling thunder that was ready to take over in my brain.” So I rose up, charged myself up “enough is enough.” My mother had already said a prayer of favor  over me. She blessed me right from the day I was conceived. “You shall not die before your time, you shall live to fulfill  your purpose on earth; No man anywhere will deny you of your dues, the harvest of your planting

AWAKENING: STORIES UNTOLD, STORIES UNHEARD AND STORIES UNREAD

  Chapter one Correct me if I am wrong, but I remember all the words you like to say behind closed doors. She whispered in my ear “I take you as you are and you will be. I won’t try to change you but I will ride out change with you. I see you and I will never ask you to be less or more.” With words so charming and full of meaning, that’s how she destroyed me. I have been awed and terrified by the experience of being in love to the extent that when it’s love, I’d rather close the book and put it back on the shelf. I do not know how to hate no matter how much I have been wronged. I met Tuseke when I had gone for my usual check-up at the hospital. She was there to visit her grandmother who was gravely ill and on admission. She had asked for directions to get to the elderly female ward, that was just the same way to Doctor Mayepi’s office. My all time go to health practitioner. We walked hand in hand and talked about a few things on science and medicine. She hated being a

LET'S TALK ABOUT SGBV TODAY!! (Sexual and Gender Based Violence)

SGBV = Sexual and Gender Based Violence is violence committed against a person because of his/her sex or gender. Books and experts have it that SGBV is more of forcing another person to do something against their will through violence, coercion, threats, deception, cultural expectations or economic means. ü   Realistically, Sexual and Gender Based Violence is pervasive and there are a series of consequences for victims and their families. To fight SGBV there should be a channel of measures and efforts, awareness campaigns and Support Services for Survivors (SSS method), there’s a need to come up with an inclusive and safe environment to promote the respect for all genders as a way of preventing and responding to SGBV. ü   The painful reality of SGBV is that it could have been any one of us or it has been so many of us. Voices are really pervasive in discussions about SGBV and it has shifted responsibility off of the group on who is committing or perpetrating the vast majority o

LET’S TALK ABOUT “HEALING” TODAY!!

  Before and After everything else, Healing comes first. You heal before you take a new step, and you heal after you meet the chaos and catastrophe. Healing is a deeply personal journey. Realistically, there’s nothing like a one-size-fits-all approach to healing. If your path looks different from others, don’t be disheartened; embrace your own journey and trust that it’s leading you exactly where you need to be. No one knows how much you’ve been through, the paths and routes you’ve been to or you’ve had to take. I read something that said; “May the quality of people you attract be a reflection of the healing and hard work you’ve put into yourself over time.” No matter how much you wish you could, there’s no way you can control how another person feels or thinks about you. That’s why it is important to surround yourself with people who are committed to understand who you truly are. The kind of people that are soft and gentle with your heart and soul, the ones who will let

LETTERS TO HIM

  Dearest Aku; I wrote this note to gently remind myself that I am going to be okay even if I don’t believe that I will. There's Philophobia and Pistanthrophobia within me. I don’t know much about love, but I know you. You are not the first person that I have confused for home. I am too real for people and I believe that’s the reason why I haven’t found love yet, everyone I meet is either fake or full of themselves. I know some things are just not meant to work out no matter how much you want them to, and some moments are meant to be brief, forcing them only harms us. I get it. I read somewhere that said; “It’s kind of hard to love someone else when the one you once loved gave you no reason to love again” and that’s exactly you and me. You know; When I like someone, I go too hard. I am too available, too giving, too loyal, too thoughtful and too reliable - hoping it gets reciprocated. Do you remember when I said; “I will peel off all my skin away if that’s how much you want me to s